YouVersion Logo
Search Icon

Marko 13:7

Marko 13:7 CCL

Pamene mudzamva zankhondo ndi mbiri zankhondo, musadzadzidzimuke. Zinthu zotere ziyenera kuchitika, koma sikuti chimaliziro chafika kale ayi.

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 13:7