YouVersion Logo
Search Icon

Marko 13:11

Marko 13:11 CCL

Nthawi iliyonse pamene mwamangidwa ndi kuyimbidwa mlandu, musadandaule za zimene mudzanena. Zimene mudzapatsidwe pa nthawiyo yankhulani; pakuti sindinu amene mudzayankhula, koma Mzimu Woyera.

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 13:11