YouVersion Logo
Search Icon

Marko 10:6-8

Marko 10:6-8 CCL

Koma pachiyambi cha chilengedwe, Mulungu ‘analenga iwo, mwamuna ndi mkazi.’ ‘Pa chifukwa ichi mwamuna adzasiya abambo ake ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake, ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi.’ Potero sali awirinso, koma mmodzi.

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 10:6-8