YouVersion Logo
Search Icon

Marko 1:10-11

Marko 1:10-11 CCL

Pamene Yesu ankatuluka mʼmadzi, anaona kumwamba kukutsekuka ndipo Mzimu Woyera akutsikira pa Iye ngati nkhunda. Ndipo Mawu anamveka kuchokera kumwamba: “Iwe ndiwe Mwana wanga wokondedwa; ndipo ndikondwera nawe.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 1:10-11