YouVersion Logo
Search Icon

Mateyu 9:35

Mateyu 9:35 CCL

Yesu anayendayenda mʼmizinda yonse ndi mʼmidzi, kuphunzitsa mʼmasunagoge awo, nalalikira Uthenga Wabwino wa ufumu ndi kuchiritsa nthenda zawo zonse ndi zofowoka za mʼmatupi mwawo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mateyu 9:35