YouVersion Logo
Search Icon

Mateyu 8:26

Mateyu 8:26 CCL

Iye anawayankha kuti, “Inu achikhulupiriro chochepa, chifukwa chiyani mukuchita mantha?” Ndipo anayimirira nadzudzula mphepoyo ndi mafunde ndipo panali bata lalikulu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mateyu 8:26