YouVersion Logo
Search Icon

Mateyu 7:3-4

Mateyu 7:3-4 CCL

“Chifukwa chiyani iwe uyangʼana kachitsotso ka mʼdiso la mʼbale wako koma susamalira chimtengo chili mʼdiso mwako? Kodi unganene bwanji kwa mʼbale wako kuti, ‘Ndikuchotse kachitsotso mʼdiso mwako,’ pamene nthawi zonse chimtengo uli nacho mʼdiso mwako?

Free Reading Plans and Devotionals related to Mateyu 7:3-4