YouVersion Logo
Search Icon

Mateyu 6:14-15

Mateyu 6:14-15 CCL

Ngati inu mukhululukira anthu pamene akuchimwirani, Atate anu akumwamba adzakukhululukirani. Koma ngati inu simukhululukira anthu zolakwa zawo, Atate anunso sadzakukhululukirani machimo anu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mateyu 6:14-15