YouVersion Logo
Search Icon

Mateyu 19:29

Mateyu 19:29 CCL

Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mateyu 19:29