Mateyu 16:15-16
Mateyu 16:15-16 CCL
Iye anafunsa kuti, “Nanga inuyo mumati ndine yani?” Simoni Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo.”
Iye anafunsa kuti, “Nanga inuyo mumati ndine yani?” Simoni Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo.”