YouVersion Logo
Search Icon

Mateyu 15:8-9

Mateyu 15:8-9 CCL

“ ‘Anthu awa amandilemekeza Ine ndi milomo yawo, koma mitima yawo ili kutali ndi Ine. Amandilambira Ine kwachabe ndi kuphunzitsa malamulo ndi malangizo a anthu.’ ”

Free Reading Plans and Devotionals related to Mateyu 15:8-9