Mateyu 15:25-27
Mateyu 15:25-27 CCL
Mayiyo anabwera ndi kugwada pamaso pake, nati, “Ambuye ndithandizeni!” Iye anayankha kuti, “Sibwino kutenga chakudya cha ana ndi kuponyera agalu.” Mayiyo anati, “Inde Ambuye. Komatu ngakhale agalu amadya nyenyeswa zimene zimagwa kuchokera pa tebulo la mbuye wawo.”





