YouVersion Logo
Search Icon

Mateyu 13:19

Mateyu 13:19 CCL

Pamene aliyense akumva uthenga wa ufumu koma sawuzindikira, woyipayo amabwera ndi kuchotsa zimene zafesedwa mu mtima mwake. Iyi ndi mbewu yofesedwa mʼmbali mwa njira.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mateyu 13:19