YouVersion Logo
Search Icon

Luka 8:25

Luka 8:25 CCL

Iye anafunsa ophunzira ake kuti, “Chikhulupiriro chanu chili kuti?” Koma pogwidwa ndi mantha ndi kudabwa anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Uyu ndi ndani? Iye alamulira ngakhale mphepo ndi madzi, ndipo zimumvera Iye.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Luka 8:25