YouVersion Logo
Search Icon

Luka 8:15

Luka 8:15 CCL

Koma mbewu za pa nthaka yabwino zikuyimira anthu amene ali ndi mtima woona ndi wabwino, amene amamva mawu nawasunga, ndipo amalimbikira mpaka amabala zipatso.

Free Reading Plans and Devotionals related to Luka 8:15