YouVersion Logo
Search Icon

Luka 7:47-48

Luka 7:47-48 CCL

Tsono, ndikukuwuza iwe, machimo ake amene ndi ambiri akhululukidwa, monga chaonetsera chikondi chake chachikulu. Koma iye amene wakhululukidwa zochepa amakonda pangʼono.” Kenaka anati kwa mayiyo, “Machimo ako akhululukidwa.”

Verse Image for Luka 7:47-48

Luka 7:47-48 - Tsono, ndikukuwuza iwe, machimo ake amene ndi ambiri akhululukidwa, monga chaonetsera chikondi chake chachikulu. Koma iye amene wakhululukidwa zochepa amakonda pangʼono.”
Kenaka anati kwa mayiyo, “Machimo ako akhululukidwa.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Luka 7:47-48