YouVersion Logo
Search Icon

Luka 7:38

Luka 7:38 CCL

Iye anayimirira kumbuyo kwa Yesu pa mapazi ake akulira, nayamba kumadontheza misozi pa mapazi ake. Ndipo iye anapukuta mapaziwo ndi tsitsi lake, nawapsompsona ndi kuwathira mafuta onunkhirawo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Luka 7:38