YouVersion Logo
Search Icon

Levitiko 23:3

Levitiko 23:3 CCL

“ ‘Pa masiku asanu ndi limodzi muzigwira ntchito, koma tsiku lachisanu ndi chiwiri ndi Sabata lopuma, tsiku la msonkhano wopatulika. Kulikonse kumene inu mukukhala musamagwire ntchito iliyonse tsiku limeneli popeza ndi tsiku la Sabata la Yehova.

Free Reading Plans and Devotionals related to Levitiko 23:3