Bible App logo
Search Icon

Maliro 2:19

Maliro 2:19 CCL

Dzuka, fuwula usiku, pamene alonda ayamba kulondera; khuthula mtima wako ngati madzi pamaso pa Ambuye. Kweza manja ako kwa Iye chifukwa cha miyoyo ya ana ako, amene akukomoka ndi njala mʼmisewu yonse ya mu mzinda.

Video for Maliro 2:19

Free Reading Plans and Devotionals related to Maliro 2:19