Bible App logo
Search Icon

Maliro 1:1

Maliro 1:1 CCL

Haa! Mzinda uja wasiyidwa wokhawokha, umene kale unali wodzaza ndi anthu! Kale unali wotchuka pakati pa mitundu ya anthu! Tsopano wasanduka ngati mkazi wamasiye. Kale unali mfumukazi ya onse pa dziko lapansi, tsopano wasanduka kapolo.

Video for Maliro 1:1

Free Reading Plans and Devotionals related to Maliro 1:1