YouVersion Logo
Search Icon

Yohane 4:23

Yohane 4:23 CCL

Koma nthawi ikubwera ndipo yafika kale tsopano pamene opembedza woona adzapembedza Atate mu mzimu ndi mʼchoonadi, pakuti opembedza otere ndiwo amene Atate akuwafuna.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yohane 4:23