YouVersion Logo
Search Icon

Yeremiya 8:7

Yeremiya 8:7 CCL

Mbalame yotchedwa kakowa ija imadziwa nthawi yake mlengalenga. Koma nkhunda, namzeze ndi chingalu zimadziwa nthawi yonyamukira ulendo, koma anthu anga sadziwa malamulo a Yehova.

Video for Yeremiya 8:7