YouVersion Logo
Search Icon

Yeremiya 7:22-23

Yeremiya 7:22-23 CCL

Pakuti pamene ndinatulutsa makolo anu ku Igupto ndi kuyankhula nawo, sindinawalamulire kuti azipereka nsembe zopsereza kapena nsembe zinazo, koma ndinawalamula kuti: Mverani Ine, ndipo ndidzakhala Mulungu wanu ndipo inu mudzakhala anthu anga. Muzitsata zonse zimene ndakulamulirani, ndipo zinthu zidzakuyenderani bwino.

Video for Yeremiya 7:22-23

Free Reading Plans and Devotionals related to Yeremiya 7:22-23