YouVersion Logo
Search Icon

Yeremiya 6:10

Yeremiya 6:10 CCL

Kodi ndiyankhule ndi yani ndi kumuchenjeza? Ndinene mawu ochenjeza kwa yani kuti amve? Makutu awo ndi otsekeka kotero kuti sangathe kumva. Mawu a Yehova ndi onyansa kwa iwo; sasangalatsidwa nawo.

Video for Yeremiya 6:10