Bible App logo
Search Icon

Yeremiya 32:39-40

Yeremiya 32:39-40 CCL

Ndidzawapatsa mtima umodzi ndi khalidwe limodzi kotero kuti azidzandiopa nthawi zonse ndipo iwo pamodzi ndi zidzukulu zawo zinthu zidzawayendera bwino. Ndidzachita nawo pangano losatha: sindidzaleka kuwachitira zabwino, ndipo ndidzawapatsa mtima woti azidzandiopa, kuti asadzandisiyenso.

Video for Yeremiya 32:39-40

Free Reading Plans and Devotionals related to Yeremiya 32:39-40