YouVersion Logo
Search Icon

Yeremiya 20:11

Yeremiya 20:11 CCL

Koma Yehova ali nane, ndiye wankhondo wamphamvu. Nʼchifukwa chake ondizunza adzalephera ndipo sadzandipambana. Adzachita manyazi kwambiri chifukwa sadzapambana. Manyazi awo sadzayiwalika konse.

Video for Yeremiya 20:11

Free Reading Plans and Devotionals related to Yeremiya 20:11