YouVersion Logo
Search Icon

Yeremiya 2:11

Yeremiya 2:11 CCL

Kodi ulipo mtundu wa anthu uliwonse umene unasinthapo milungu yake? (Ngakhale kuti si milungu nʼkomwe). Koma anthu anga asinthitsa Mulungu wawo waulemerero ndi mafano achabechabe.

Video for Yeremiya 2:11

Free Reading Plans and Devotionals related to Yeremiya 2:11