YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 66:1

Yesaya 66:1 CCL

Yehova akuti, “Kumwamba ndi mpando wanga waufumu ndipo dziko lapansi ndilo chopondapo mapazi anga. Tsono nyumba ili kuti yomwe mundimangire, ndipo malo ali kuti amene inu mungandikonzere kuti ndizipumuliramo?

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 66:1