YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 65:22

Yesaya 65:22 CCL

Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo, kapena kudzala ndi ena nʼkudya. Pakuti anthu anga adzakhala ndi moyo wautali ngati mitengo. Osankhidwa anga adzakondwera ndi ntchito ya manja awo nthawi yayitali.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 65:22