YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 63:7

Yesaya 63:7 CCL

Ndidzafotokoza za kukoma mtima kwa Yehova, ntchito zimene Iye ayenera kutamandidwa. Ndidzatamanda Yehova chifukwa cha zonse zimene watichitira. Inde, mwa chifundo ndi kukoma mtima kwake Yehova wachitira nyumba ya Israeli zinthu zabwino zambiri.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 63:7