YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 62:5

Yesaya 62:5 CCL

Monga mnyamata amakwatira namwali, momwenso mmisiri wodzakumanga adzakukwatira; monga mkwati amakondwera ndi mkwatibwi, chonchonso Mulungu adzakondwera nawe.