YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 60:21

Yesaya 60:21 CCL

Ndipo anthu ako onse adzakhala olungama ndipo dzikolo lidzakhala lawo mpaka muyaya. Iwo ndi mphukira imene Ine ndayidzala, ntchito ya manja anga, kuti aonetse ulemerero wanga.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 60:21