YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 54:9

Yesaya 54:9 CCL

“Kwa ine zimenezi zili ngati mmene zinalili mʼnthawi ya Nowa. Monga ndinalumbira nthawi imeneyo kuti sindidzawononganso dziko lapansi ndi madzi. Kotero tsopano ndalumbira kuti sindidzakupseraninso mtima, sindidzakudzudzulaninso.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 54:9