YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 54:5

Yesaya 54:5 CCL

Pakuti Mlengi wako ali ngati mwamuna wako, dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse. Woyerayo wa Israeli ndiye Mpulumutsi wanu; dzina lake ndi Mulungu wa dziko lonse lapansi.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 54:5