YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 54:4

Yesaya 54:4 CCL

“Usachite mantha; sadzakunyozanso. Usakhumudwe; sudzapeputsidwanso. Udzayiwala za manyazi zimene zinakuchitikira nthawi ya unyamata wako ndipo za manyazi zimene zinakuchitikira pa nthawi ya umasiye wako sudzazikumbukanso.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 54:4