YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 53:8

Yesaya 53:8 CCL

Atatha kumugwira mwankhanza ndikumuyimba mlandu, kenaka anapita naye kukamupha. Ndipo ndani amene analabadirako za zidzukulu zake, poona kuti iye anachotsedwa mʼdziko la anthu amoyo? Ndani anaganizirapo poona kuti iye anakanthidwa chifukwa cha zolakwa za anthu anga?

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 53:8