YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 53:7

Yesaya 53:7 CCL

Anthu anamuzunza ndi kumusautsa, koma sanayankhule kanthu. Monga mwana wankhosa wopita naye kokamupha amachitira, kapena monga nkhosa imakhalira duu poyimeta, momwemonso iye sanatsekule pakamwa pake.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 53:7