YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 53:4

Yesaya 53:4 CCL

Ndithudi, iye anamva zowawa mʼmalo mwa ife; ndipo anasautsidwa mʼmalo mwathu. Koma ife tinkaganiza kuti ndi Mulungu amene akumulanga, kumukantha ndi kumusautsa.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 53:4