YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 53:11

Yesaya 53:11 CCL

Atatha mazunzo a moyo wake, adzaona kuwala, ndipo adzakhutira. Mwa nzeru zake mtumiki wanga wolungamayo adzalungamitsa anthu ambiri, popeza adzasenza zolakwa zawo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 53:11