YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 52:7

Yesaya 52:7 CCL

Ngokongoladi mapazi a amithenga obweretsa nkhani yabwino amene akuyenda pa mapiri. Iwo akukubweretserani nkhani zabwino za mtendere, chisangalalo ndi chipulumutso. Iwo akubwera kudzawuza anthu a ku Ziyoni kuti, “Mulungu wako ndi mfumu!”

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 52:7