YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 43:4

Yesaya 43:4 CCL

Popeza kuti ndiwe wamtengowapatali wolemekezeka ndi wapamtima panga, ndipo chifukwa ndimakukonda, ndidzapereka anthu mʼmalo mwa iwe, ndidzapereka mitundu ya anthu pofuna kuwombola moyo wako.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 43:4