YouVersion Logo
Search Icon

Hoseya 3:1

Hoseya 3:1 CCL

Yehova anati kwa ine, “Pita kamukondenso mkazi wako, ngakhale ali pa chibwenzi ndi wina ndi kuti ndi wachigololo. Mukonde iyeyo monga momwe Yehova amakondera Aisraeli, ngakhale iwo amapita kukapembedza milungu ina ndi kukonda nsembe za keke zamphesa zowuma.”

Related Videos

Free Reading Plans and Devotionals related to Hoseya 3:1