Hoseya 2:19-20
Hoseya 2:19-20 CCL
Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya; ndidzakutomera mwachilungamo, mwaungwiro, mwachikondi ndi mwachifundo. Ndidzakutomera mokhulupirika ndipo udzadziwa Yehova.
Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya; ndidzakutomera mwachilungamo, mwaungwiro, mwachikondi ndi mwachifundo. Ndidzakutomera mokhulupirika ndipo udzadziwa Yehova.