YouVersion Logo
Search Icon

Hagai 1:5-6

Hagai 1:5-6 CCL

Tsono zimene Yehova Wamphamvuzonse akunena ndi izi, “Ganizirani bwino njira zanu. Mwadzala zambiri, koma mwakolola zochepa. Mumadya, koma simukhuta. Mumamwa, koma ludzu lanu silitha. Mumavala, koma simumva kutentha. Mumalandira malipiro, koma ndalama zanu zimatha ngati mwaziyika mʼthumba lobowoka.”

Related Videos

Free Reading Plans and Devotionals related to Hagai 1:5-6