Genesis 49:22-23
Genesis 49:22-23 CCL
“Yosefe ali ngati mtengo wobereka zipatso, mtengo wobereka zipatso pafupi ndi kasupe, nthambi zake zimayanga pa chipupa cha mwala. Alenje a uta anamuchita chiwembu mwankhanza; anamuthamangitsa ndi mauta awo.
“Yosefe ali ngati mtengo wobereka zipatso, mtengo wobereka zipatso pafupi ndi kasupe, nthambi zake zimayanga pa chipupa cha mwala. Alenje a uta anamuchita chiwembu mwankhanza; anamuthamangitsa ndi mauta awo.