YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 47:9

Genesis 47:9 CCL

Yakobo anayankha kuti, “Zaka za maulendo anga zakwana 130. Zaka za moyo wanga ndi zowerengeka, komanso zakhala zaka za masautso. Zaka za moyo wanga sizingafanane ndi zaka za moyo wa makolo anga.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 47:9