YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 42:6

Genesis 42:6 CCL

Pakuti Yosefe anali nduna yayikulu yolamulira dziko la Igupto, ndiye kuti analinso amene ankagulitsa tirigu kwa anthu onse. Choncho abale ake a Yosefe nawonso anabwera, ndipo anamugwadira pansi.

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 42:6