YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 40:8

Genesis 40:8 CCL

Iwo anayankha, “Tonse awiri talota maloto, koma palibe wotitanthauzira malotowo.” Pamenepo Yosefe anawawuza kuti, “Ndi Mulungu yekha amene amapereka matanthauzo a maloto. Uzeni ine maloto anu.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 40:8