YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 38:9

Genesis 38:9 CCL

Koma Onani anadziwa kuti mwanayo sadzakhala wake. Choncho nthawi zonse pamene amagona naye mkaziyo, ankatayira umuna pansi kuti asamuberekere mwana mʼbale wake.

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 38:9