YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 32:10

Genesis 32:10 CCL

Ine siwoyenera kulandira kukoma mtima kwanu ndi kukhulupirika kwanu kumene mwaonetsa wantchito wanu. Ndinali ndi ndodo yokha pamene ndinawoloka Yorodani uyu koma tsopano ndili ndi magulu awiri.

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 32:10